Luka 4:36 BL92

36 Ndipo anthu onse anadabwa, nalankhulana wina ndi mnzace, nanena, Mau amenewa ali otani? cifukwa ndi ulamuliro ndi mphamvu angolamulira mizimu yonyansa, ndipo ingoturuka.

Werengani mutu wathunthu Luka 4

Onani Luka 4:36 nkhani