Luka 4:41 BL92

41 Ndi ziwanda zomwe zinaturuka mwa ambiri, ndi kupfuula, kuti, Inu ndinu Mwana wa Mulungu. Ndipo iye anazidzudzula, wosazilola kulankhula, cifukwa zinamdziwa kuti iye ndiye Kristu.

Werengani mutu wathunthu Luka 4

Onani Luka 4:41 nkhani