Luka 7:32 BL92

32 Angofanana ndi ana akukhala pamsika, ndi kuitanizana wina ndi mnzace, ndi kunena, Ife tinakulizirani citoliro, ndipo inu simunabvina ai; tinabuma maliro, ndimo simunalira ai.

Werengani mutu wathunthu Luka 7

Onani Luka 7:32 nkhani