Luka 7:47 BL92

47 Cifukwa cace, ndinena kwa iwe, Macimo ace, ndiwo ambiri, akhululukidwa; cifukwa anakonda kwambiri; koma munthu amene anamkhululukira pang'ono, iye akonda pang'ono.

Werengani mutu wathunthu Luka 7

Onani Luka 7:47 nkhani