Luka 8:16 BL92

16 Ndipo palibe munthu, atayatsa, nyali, aibvundikira ndi cotengera, kapena kuiika pansi pa kama; koma aiika pacoikapo, kuti iwo akulowamo aone kuunikaku.

Werengani mutu wathunthu Luka 8

Onani Luka 8:16 nkhani