Luka 9:22 BL92

22 nati, Kuyenera kuti Mwana wa munthu amve zowawa zambiri, ndi kukanidwa ndi akuru, ndi ansembe akuru, ndi alembi, ndi kuphedwa, ndi kuuka tsiku lacitatu.

Werengani mutu wathunthu Luka 9

Onani Luka 9:22 nkhani