Mateyu 16:3 BL92

3 Ndipo m'mawa, Lero nkwa mphepo; popeza thambo liri la ceza codera. Mudziwa kuzindikira za pa nkhope ya thambo; koma zizindikiro za nyengo yin o, simungathe kuzindikira.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 16

Onani Mateyu 16:3 nkhani