Mateyu 25:44 BL92

44 Pomwepo iwonso adzayankha kuti, Ambuye, tinakuonani liti wanjala, kapena waludzu, kapena mlendo, kapena wamarisece, kapena m'nyumba yandende, ndipo ife sitinakutumikirani Inu?

Werengani mutu wathunthu Mateyu 25

Onani Mateyu 25:44 nkhani