Mateyu 25:45 BL92

45 Pomwepo Iye adzayankha iwo kuti, Indetu ndinena kwa inu, Cifukwa munalibe kucitira ici mmodzi wa awa ang'onong'ono, munalibe kundicitira ici Ine.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 25

Onani Mateyu 25:45 nkhani