Mateyu 27:24 BL92

24 Koma Pilato poona kuti sanafitse, koma kuti linapambana phokoso, anatenga madzi, nasamba manja pamaso pa khamulo, nati, Ine ndiribe kucimwira mwazi wa munthu uyu wolungama, mudzionere nokha.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 27

Onani Mateyu 27:24 nkhani