Mateyu 8:13 BL92

13 Ndipo Yesu anati kwa kenturiyoyo, Pita, kukhale kwa iwe monga unakhulupirira. Ndipo anaciritsidwa mnyamatayo nthawi yomweyo.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 8

Onani Mateyu 8:13 nkhani