1 Samueli 1:17 BL92

17 Pamenepo Eli anayankha nati, Pita ndi mtendere; ndipo Mulungu wa Israyeli akupatse copempha cako unacipempha, kwa iye.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 1

Onani 1 Samueli 1:17 nkhani