1 Samueli 10:21 BL92

21 Nayandikizitsa pfuko la Benjamini, banja ndi banja, ndipo banja la Amatiri linasankhidwa; nasankhidwa Sauli mwana wa Kisi. Koma pamene anamfuna, anapeza palibe.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 10

Onani 1 Samueli 10:21 nkhani