28 Ndipo wina wa anthuwo anayankha, nati, Atate wanu analangiza anthu kolimba ndi lumbiro, ndi kuti, Wotembereredwa iye wakudya lero cakudya. Ndipo anthuwo analema.
Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 14
Onani 1 Samueli 14:28 nkhani