41 Cifukwa cace Sauli ananena ndi Yehova, Mulungu wa Israyeli, muonetse coonadi. Ndipo maere anagwera Sauli ndi Jonatani; koma anthuwo anapulumuka.
Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 14
Onani 1 Samueli 14:41 nkhani