1 Samueli 17:57 BL92

57 Ndipo pamene Davide anabwera, atapha Mfilistiyo, Abineri anamtenga, nafika naye pamaso pa Sauli, mutu wa Mfilistiyo uli m'dzanja lace.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 17

Onani 1 Samueli 17:57 nkhani