1 Samueli 18:6 BL92

6 Ndipo kunali pakudza iwo, pamene Davide anabwera atapha Afilistiwo, anthu akazi anaturuka m'midzi yonse ya Israyeli, ndi kuyimba ndi kubvina, kuti akakomane ndi mfumu Sauli, ndi malingaka, ndi cimwemwe, ndi zoyimbira.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 18

Onani 1 Samueli 18:6 nkhani