13 Mulungu alange Jonatani, ndi kuonjezapo, ngati atate wanga akondwera kukucitira coipa, ine osakuululira, ndi kukucotsa kuti upite mumtendere; ndipo Yehova akhale nawe, monga anakhala naye atate wanga.
Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 20
Onani 1 Samueli 20:13 nkhani