34 Pamenepo Jonatani anauka pagome wolunda ndithu, osadya kanthu tsiku laciwiri la mwezi, pakuti mtima wace unali ndi cisoni cifukwa ca Davide, popeza atate wace anamcititsa manyazi.
Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 20
Onani 1 Samueli 20:34 nkhani