11 Ndipo anyamata a Akisi ananena naye, Uyu si Davide mfumu ya dzikolo kodi? Sanathirirana mang'ombe za iye kodi m'magule ao, ndi kuti,Sauli anapha zikwi zace,Koma Davide zikwi zace zankhani?
Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 21
Onani 1 Samueli 21:11 nkhani