11 Pamenepo mfumu anatuma mthenga kukaitana Ahimeleki wansembeyo, mwana wa Ahitubu, ndi banja lonse la atate wace, ansembe a ku Nobi; ndipo iwo onse anafika kwa mfumu.
Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 22
Onani 1 Samueli 22:11 nkhani