22 Mukanitu kuti mukadziwitse ndithu, ndi kudziwa ndi kuona mbuto m'mene akhalitsa, ndi amene adamuona m'menemo; cifukwa anandiuza kuti iye acita mocenjera ndithu.
Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 23
Onani 1 Samueli 23:22 nkhani