1 Samueli 25:31 BL92

31 mudzakhala opanda cakudodoma naco, kapena cakusauka naco mtima wa mbuye wanga, cakuti munakhetsa mwazi wopanda cifukwa, kapena kuti mbuye wanga anabwezera cilango; ndipo Yehova akadzacitira mbuye wanga zabwino, pamenepo mukumbukile mdzakazi wanu.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 25

Onani 1 Samueli 25:31 nkhani