1 Samueli 3:17 BL92

17 Ndipo anati, Anakuuza cinthu canji? Usandibisire ine. Mulungu akulangendi kuonjezapo, ngati undibisira cimodzi ca zonse zija adanena nawe.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 3

Onani 1 Samueli 3:17 nkhani