26 Ndipo pamene Davide anafika ku Zikilaga, anatumizako za zofunkhazo kwa akuru a Yuda, ndiwo abwenzi ace, nati, Siyi mphatso yanu ya zofunkha za adani a Yehova.
Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 30
Onani 1 Samueli 30:26 nkhani