1 Samueli 5:9 BL92

9 Ndipo kunali atafika nalo, dzanja la Yehova linatsutsa mudziwo ndi kusautsa kwakukuru; ndipo anazunza anthu a mudziwo, akuru ndi ang'ono; ndi mafundo anawabuka.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 5

Onani 1 Samueli 5:9 nkhani