1 Samueli 7:2 BL92

2 Ndipo kunali, kuti likasalo linakhala nthawi yaikuru m'Kiriati-yearimu; popeza linakhalako zaka makumi awiri; ndipo banja lonse la Israyeli linalirira Yehova.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 7

Onani 1 Samueli 7:2 nkhani