2 Mafumu 15:25 BL92

25 Ndipo Peka mwana wa Remaliya, kazembe wace, anamcitira ciwembu, nawakantha limodzi mfumu ndi Arigobo ndi Ariye m'Samariya, m'nsanja ya ku nyumba ya mfumu; pamodzi ndi iye panali amuna makumi asanu a Gileadi; ndipo anamupha, nakhala mfumu m'malo mwace.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 15

Onani 2 Mafumu 15:25 nkhani