2 Mafumu 15:9 BL92

9 Nacita iye coipa pamaso pa Yehova, monga adacita makolo ace; sanaleka zolakwa zace za Yerobiamu mwana wa Nebati, zimene analakwitsa nazo Israyeli.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 15

Onani 2 Mafumu 15:9 nkhani