2 Mafumu 17:21 BL92

21 Pakuti anang'amba Israyeli, kumcotsa ku nyumba ya Davide; ndipo anamlonga mfumu Yerobiamu mwana wa Nebati; Yerobiamu naingitsa Israyeli asatsate Yehova, nawalakwitsa kulakwa kwakukuru.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 17

Onani 2 Mafumu 17:21 nkhani