2 Ndipo Eliya anati kwa Elisa, Ukhale pompano pakuti Yehova wandituma ndimke ku Beteli. Nati Elisa, Pali Mulungu, pali inu, sindikusiyani. Motero anatsikira iwo ku Beteli.
Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 2
Onani 2 Mafumu 2:2 nkhani