15 Ndipo anawalondola mpaka ku Yordano; ndipo taonani, m'njira monse munadzala ndi zobvala ndi akatundu adazitaya Aaramu m'kufulumira kwao. Nibwera mithenga, nifotokozera mfumu.
Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 7
Onani 2 Mafumu 7:15 nkhani