Luka 10:40 BL92

40 Koma Marita anatekeseka ndi kutumikira kwambiri; ndipo anadzako nati, Ambuye, kodi simusamala kuti mbale wanga anandisiya nditumikire ndekha? Mumuuze tsono kuti andithandize.

Werengani mutu wathunthu Luka 10

Onani Luka 10:40 nkhani