Luka 11:19 BL92

19 Koma ngati Ine ndimaturutsa ziwanda ndi Beelzebule, ana anu aziturutsa ndi yani? Mwa ici iwo adzakhala oweruza anu.

Werengani mutu wathunthu Luka 11

Onani Luka 11:19 nkhani