Luka 15:20 BL92

20 Ndipo iye ananyamuka, nadza kwa atate wace. Koma pakudza iye kutali, atate wace anamuona, nagwidwa cifundo, nathamanga, namkupatira pakhosi pace, nampsompsonetsa.

Werengani mutu wathunthu Luka 15

Onani Luka 15:20 nkhani