Luka 17:6 BL92

6 Koma Ambuye anati, Mukakhala naco cikhulupiriro ngati kambeu kampiru, mukanena kwa mtengo uwu wamkuyu, Uzulidwe, nuokedwe m'nyanja; ndipo ukadamvera inu.

Werengani mutu wathunthu Luka 17

Onani Luka 17:6 nkhani