Luka 19:15 BL92

15 Ndipo kunali, pakubwera iye, atalandira ufumuwo, anati aitanidwe kwa iye akapolo aja, amene adawapatsa ndalamazo, kuti adziwe umo anapindulira pocita malonda.

Werengani mutu wathunthu Luka 19

Onani Luka 19:15 nkhani