Luka 20:9 BL92

9 Ndipo iye anayamba kunena kwa anthu fanizo ili: Munthu analima munda wamphesa, naukongoletsa kwa olima munda, nanka ku dziko lina, nagonerako nthawi yaikuru.

Werengani mutu wathunthu Luka 20

Onani Luka 20:9 nkhani