Luka 22:10 BL92

10 Ndipo iye anati kwa iwo, Onani, mutalowa m'mudzi, adzakomana ndinu munthu alikusenza mtsuko wa madzi; mumtsate ameneyo kunyumba kumene akalowako iye.

Werengani mutu wathunthu Luka 22

Onani Luka 22:10 nkhani