Luka 23:46 BL92

46 Ndipo pamene Yesu anapfuula ndi mau akuru, anati, 1 Atate, m'manja mwanu ndipereka mzimu wanga. Ndipo pakutero anapereka mzimu wace.

Werengani mutu wathunthu Luka 23

Onani Luka 23:46 nkhani