Luka 24:19 BL92

19 Ndipo anati kwa iwo, Zinthu zanji? Ndipo anati kwa iye, lzi za Yesu Mnazarene, ndiye munthu mneneri wamphamvu m'nchito, ndi m'mau, pamaso pa Mulungu ndi anthu onse;

Werengani mutu wathunthu Luka 24

Onani Luka 24:19 nkhani