Luka 24:18 BL92

18 Ndipo mmodzi wa iwo, dzina lace Kleopa, anayankha nati kwa iye, Kodi iwe wekha ndiwe mlendo m'Yerusalemu ndi wosazindikira zidacitikazi masiku omwe ano?

Werengani mutu wathunthu Luka 24

Onani Luka 24:18 nkhani