49 Ndipo onani, 12 Ine nditumiza pa inu lonjezano la Atate wanga; koma khalani inu m'mudzi muno, kufikira mwabvekedwa ndi mphamvu yocokera Kumwamba.
50 Ndipo anaturuka nao kufikira ku Betaniya; nakweza manja ace, nawadalitsa.
51 Ndipo kunali, 13 pakuwadalitsa iye analekana nao, natengedwa kunka Kumwamba.
52 Ndipo 14 anamlambira iye, nabwera ku Yerusalemu ndi cimwemwe cacikuru;
53 ndipo IS anakhala ci khalire m'Kacisi, nalikuyamika Mulungu, Amen.