Luka 5:14 BL92

14 Ndipo iye anamuuzitsa, kuti asanene kwa munthu ali yense; koma ucoke, nudzionetse wekha kwa wansembe, nupereke nsembe ya pa cikonzedwe cako, monga adalamulira Mose, kukhale umboni kwa iwo.

Werengani mutu wathunthu Luka 5

Onani Luka 5:14 nkhani