Luka 8:10 BL92

10 Ndipo iye anati, Kwapatsidwa kwa inu kuzindikira zinsinsi za Ufumu wa Mulungu; koma kwa ena otsala ndinena nao mwa mafanizo; kuti pakuona sangaone, ndi pakumva sangadziwitse,

Werengani mutu wathunthu Luka 8

Onani Luka 8:10 nkhani