Luka 8:45 BL92

45 Ndipo Yesu anati, Wandikhudza Ine ndani? Koma pamene onse anakana, Petro ndi iwo akukhala naye anati, Ambuye, anthu aunyinji alikukankhana pa Inu ndi kukanikizana.

Werengani mutu wathunthu Luka 8

Onani Luka 8:45 nkhani