Luka 8:47 BL92

47 Ndipo mkaziyo pakuona kuti sanabisika, anadza ndi kunthunthumira, nagwa pamaso pace, nafotokoza pamaso pa anthu onsewo cifukwa cace ca kumkhudza iye, ndi kuti anaciritsidwa pomwepo.

Werengani mutu wathunthu Luka 8

Onani Luka 8:47 nkhani