Luka 8:8 BL92

8 Ndipo zina zinagwa pa nthaka yokoma, ndipo zinamera, ndi kupatsa zipatso zamakumikhumi. Pakunena iye izi anapfuula, iye amene ali ndi makutu akumva amve.

Werengani mutu wathunthu Luka 8

Onani Luka 8:8 nkhani