Luka 9:26 BL92

26 Pakuti amene ali yense: adzacita manyazi cifukwa ca Ine ndi mau anga, Mwana wa munthu adzacita manyazi cifukwa ca iye, pamene adzafika ndi ulemerero wace ndi wa Atate, ndi wa angelo oyera.

Werengani mutu wathunthu Luka 9

Onani Luka 9:26 nkhani