Luka 9:28 BL92

28 Ndipo pamene padatha ngati masiku asanu ndi atatu atanena mau amenewa, Iye anatenga Petro ndi Yohane ndi Yakobo apite naye, nakwera m'phiri kukapemphera.

Werengani mutu wathunthu Luka 9

Onani Luka 9:28 nkhani